Matthew 16:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Yesu adaŵafunsa kuti, “Nanga inuyo, mumati ndine yani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye ananena kwa iwo, Koma inu mutani kuti Ine ndine yani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anafunsa kuti, “Nanga inuyo mumati ndine yani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye ananena kwa iwo, Koma inu mutani kuti Ine ndine yani?