Matthew 17:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo ophunzira aja adazindikira kuti ankaŵauza za Yohane Mbatizi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomwepo ophunzira anazindikira kuti analankhula nao za Yohane Mbatizi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo ophunzira anazindikira kuti amawawuza za Yohane Mʼbatizi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomwepo ophunzira anazindikira kuti analankhula nao za Yohane Mbatizi.