Matthew 17:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Yesu adabwera, naŵakhudza nkunena kuti, “Dzukani, musachite mantha.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesu anadza, nawakhudza nati, Ukani, musaopa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Yesu anabwera nawakhudza nati, “Dzukani, musaope.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesu anadza, nawakhudza nati, Ukani, musaopa,