Matthew 18:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Yesu adaitana mwana namuimiritsa pakati pao,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene Yesu anaitana kamwana, anakaimitsa pakati pao,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anayitana kamwana kakangʼono ndi kukayimiritsa pakati pawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene Yesu anaitana kamwana, anakaimitsa pakati pao,