Matthew 18:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atangoyamba kumene, adabwera ndi wantchito wina amene anali ndi ngongole ya ndalama zochuluka kwabasi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene anayamba kuwerengera, anadza kwa iye ndi wina wamangawa wa ndalama za matalente zikwi khumi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atangoyamba kulandira, anamubweretsa munthu kwa iye amene anakongola ndalama 10,000.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene anayamba kuwerengera, anadza kwa iye ndi wina wamangawa wa ndalama za matalente zikwi khumi.