Matthew 20:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye iwowo polandira, adayamba kuŵiringula,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma m'mene iwo analilandira, anaderera kwa mwini banja,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atalandira, anayamba kuderera kwa mwini mundayo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma m'mene iwo analilandira, anaderera kwa mwini banja,