Matthew 20:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaima, naŵaitana, nkuŵafunsa kuti, “Kodi mukufuna kuti ndikuchitireni chiyani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikuchitireni chiyani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anayima ndi kuwayitana ndipo anawafunsa kuti, “Mukufuna ndikuchitireni chiyani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikucitireni ciani?