Matthew 21:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati mukhala ndi chikhulupiriro, zonse zimene mungapemphe kwa Mulungu mudzalandira.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo zinthu zilizonse mukazifunsa m'kupemphera ndi kukhulupirira, mudzazilandira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati mukhulupirira, mudzalandira chilichonse chimene muchipempha mʼpemphero.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo zinthu ziri zonse mukazifunsa m'kupemphera ndi kukhulupirira, mudzazilandira.