Matthew 22:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi ina Afarisi adakapangana zodzatapa Yesu m'kamwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka Afarisi anatuluka nakakonza njira zomupezera zifukwa Yesu mʼmawu ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwace.