Matthew 22:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Yesu podziŵa maganizo ao oipa, adati, “Bwanji kodi mukundiyesa dala, anthu achiphamasonu?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Yesu anadziwa kuipa kwao, nati, Mundiyeseranji Ine, onyenga inu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Yesu podziwa maganizo awo oyipa anati, “Inu achiphamaso, bwanji mufuna kundipezera chifukwa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Yesu anadziwa kuipa kwao, nati, Mundiyeseranji Ine, onyenga inu?