Matthew 22:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Iye adaŵafunsa kuti, “Kodi nkhopeyi ndi ya yani, ndipo dzinali ndi la yani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Iye anati kwa iwo, Ncha yani chithunzithunzi ichi, ndi kulemba kwake?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo anawafunsa kuti, “Kodi chithunzi ichi ndi malemba awa ndi za ndani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Iye anati kwa iwo, Nca yani cithunzithunzi ici, ndi kulemba kwace?