Matthew 22:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Idatuma antchito ake kuti akaŵauze anthu amene adaaitanidwa kuphwandoko kuti azibwera, anthuwo nkukana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
natumiza akapolo ake kukaitana oitanidwa kuukwati umene; ndipo iwo sanafune kudza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anatumiza antchito ake kwa amene anayitanidwa kuphwando koma anakana kubwera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
natumiza akapolo ace kukaitana oitanidwa ku ukwati umene; ndipo iwo sanafuna kudza.