Matthew 22:33 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene anthu ochuluka aja amene anali pamenepo adamva zimenezi, adadabwa kwambiri ndi zophunzitsa zake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene makamu a anthu anamva, anazizwa ndi chiphunzitso chake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Magulu a anthu atamva zimenezi, anazizwa ndi chiphunzitso chake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene makamu a anthu anamva, anazizwa ndi ciphunzitso cace.