Matthew 22:45 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngati Davide akutchula Mpulumutsi wolonjezedwa uja kuti Mbuye wake, angakhale mwana wakenso bwanji?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ngati Davide amtchula Iye Ambuye, ali mwana wake bwanji? Ndipo panalibe mmodzi anatha kumyankha mau.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati tsono Davide amamutchula ‘Ambuye,’ zingatheke bwanji kukhala mwana wake?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ngati Davide amchula Iye Ambuye, ali mwana wace bwanji? Ndipo panalibe mmodzi anatha kumyankha mau.