Matthew 22:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma oitanidwawo sadalabadireko, adangopita ku zao: wina kumunda kwake, wina ku ntchito yake yamalonda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iwo ananyalanyaza, nachoka, wina kumunda wake, wina kumalonda ake:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma iwo sanalabadire ndipo anachoka; wina anapita ku munda wake ndi wina ku malonda ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iwo ananyalanyaza, nacoka, wina ku munda wace, wina ku malonda ace: