Matthew 22:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Enawo adagwira antchito a mfumu aja naŵazunza, nkuŵapha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo otsala anagwira akapolo ake, nawachitira chipongwe, nawapha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo otsalawo anagwira antchito ake, nawazunza ndi kuwapha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo otsala anagwira akapolo ace, nawacitira cipongwe, nawapha.