Matthew 23:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma potero mukuvomera nokha kuti ndinu zidzukulu za anthu amene adapha aneneriwo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomwepo mutsimikiza nokha, kuti muli ana a iwo amene anapha aneneri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Potero mukutsimikiza kuti muli ana a iwo amene anapha aneneri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomwepo mutsimikiza nokha, kuti muli ana a iwo amene anapha aneneri.