Matthew 23:36 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndithu ndikunenetsa kuti chilango cha zonsezi chidzaŵagwera ndithu anthu amakonoŵa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Indetu ndinena kwa inu, Zinthu zonse izi zidzafika pa mbadwo uwu wamakono.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zoonadi, ndikuwuzani kuti zonsezi zidzafika pa mʼbado uno.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Indetu ndinena kwa inu, Zinthu zonse izi zidzafika pa mbadwo uwu wamakono.