Matthew 23:38 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndithu nyumba yanu yaikuluyi idzasanduka bwinja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Onani, nyumba yanu yasiyidwa kwa inu yabwinja.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taona, nyumba yako yasiyidwa ya bwinja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Onani, nyumba yanu yasiyidwa kwa inu yabwinja.