Matthew 24:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nchifukwa chake, anthu akadzakuuzani kuti, ‘Inu, Khristu ali ku chipululu,’ musadzapiteko. Kapena akadzati, ‘Ali m'kati mwa nyumba,’ musadzakhulupirire.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Onani, ali m'zipinda; musavomereze.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndiye ngati wina akuwuzani inu kuti, ‘Uyo ali ku chipululu,’ inu musapiteko; kapena akati, ‘Uyu ali kuno mʼchipinda chamʼkati,’ musakhulupirire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Onani, ali m'zipinda; musabvomereze.