Matthew 24:48 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ngati ndi wantchito woipa, mumtima mwake azidzati, ‘Mbuye wanga akuchedwa.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma kapolo woipa akanena mumtima mwake, Mbuye wanga wachedwa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo ndi woyipa, nati kwa iye yekha, ‘Mbuye wanga akuchedwa kubwera,’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma kapolo woipa akanena mumtima mwace, Mbuye wanga wacedwa;