Matthew 25:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma mkwatiyo adati, ‘Pepani, sindikukudziŵani!’ ”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma iye anayankha kuti, ‘Zoonadi, ine ndikuwuzani kuti sindikukudziwani.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani.