Matthew 25:39 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndi liti tidaamvapo kuti mukudwala kapena kuti muli m'ndende, ife nkudzakuchezetsani?’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo tinakuonani Inu liti wodwala, kapena m'nyumba yandende, ndipo tinadza kwa Inu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndi liti tinakuonani mutadwala kapena ku ndende ndipo tinakuyenderani?’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo tinakuonani Inu liti wodwala, kapena m'nyumba yandende, ndipo tinadza kwa Inu?