Matthew 25:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anamwali khumi aja adadzuka, nkuyamba kukonza nyale zao zija.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomwepo anauka anamwali onse amenewo, nakonza nyali zao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pamenepo anamwali onse anadzuka nayatsa nyale zawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomwepo anauka anamwali onse amenewo, nakonza nyali zao.