Matthew 26:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu osauka muli nawo nthaŵi zonse, koma Ine simudzakhala nane nthaŵi zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti nthawi zonse muli nao aumphawi pamodzi nanu; koma simuli ndi Ine nthawi zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Osauka mudzakhala nawo nthawi zonse, koma simudzakhala ndi Ine nthawi zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti nthawi zonse muli nao aumphawi pamodzi nanu; koma simuli ndi Ine nthawi zonse.