Matthew 26:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono ataimba nyimbo yotamanda Mulungu, onse adatuluka nkumapita ku Phiri la Olivi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene anaimba nyimbo, anatuluka kunka kuphiri la Azitona.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atayimba nyimbo, anatuluka kupita ku phiri la Olivi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene anayimba nyimbo, anaturuka kunka ku phiri la Azitona.