Matthew 26:43 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene adabwerakonso, adaŵapeza ali m'tulo, chifukwa zikope zao zinkalemera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atabweranso anawapeza ali mtulo chifukwa zikope zawo zinalemedwa ndi tulo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo.