Matthew 26:46 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Dzukani, tiyeni tizipita. Suuyu wodzandipereka uja, wafika.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ukani, timuke; taonani, iye wakundipereka wayandikira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Imirirani, tiyeni tizipita! Wondipereka Ine wafika!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ukani, timuke; taonani, iye wakundipereka wayandikira.