Matthew 26:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lina Yesu anali ku Betaniya, m'nyumba ya Simoni wotchedwa Wakhate.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene Yesu anali m'Betaniya, m'nyumba ya Simoni wakhate,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu ali ku Betaniya mʼnyumba Simoni Wakhate,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene Yesu anali m'Betaniya, m'nyumba ya Simoni wakhate,