Matthew 27:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'maŵa kutacha, akulu onse a ansembe ndi akulu a Ayuda adapanga upo kuti aphe Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pakudza mamawa, ansembe aakulu ndi akulu a anthu onse anakhala upo wakumchitira Yesu, kuti amuphe;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mmamawa, akulu a ansembe onse ndi akuluakulu anavomerezana kuti aphe Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pakudza mamawa, ansembe akuru ndi akuru a anthu onse anakhala upo wakumcitira Yesu, kuti amuphe;