Matthew 27:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Pilato adamufunsa kuti, “Kodi sukumva zonse akukunenezazi?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomwepo Pilato ananena kwa Iye, Sukumva kodi zinthu zambiri zotere akunenera Iwe?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka Pilato anamufunsa Iye kuti, “Kodi sukumva zinthu zimene akukunenerazi?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomwepo Pilato ananena kwa Iye, Sukumva kodi zinthu zambiri zotere akunenera Iwe?