Matthew 27:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adaatero chifukwa adaadziŵa kuti Yesuyo anthuwo angodzampereka chifukwa cha kaduka chabe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti anadziwa kuti anampereka Iye mwanjiru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti anadziwa kuti anamupereka Yesu chifukwa cha kaduka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti anadziwa kuti anampereka Iye mwanjiru.