Matthew 27:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adammanga, napita naye kwa Pilato, bwanamkubwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo anammanga Iye, namuka naye, nampereka Iye kwa Pilato kazembeyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anamumanga, napita naye kukamupereka kwa bwanamkubwa Pilato.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo anammanga Iye, namuka naye, nampereka Iye kwa Pilato kazembeyo.