Matthew 27:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akulu a ansembe ndi akulu a Ayuda adayamba kukakamiza anthu kupempha Pilato kuti amasule Barabasi, ndipo kuti Yesu aphedwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ansembe aakulu ndi akulu anapangira anthu kuti apemphe Barabasi, koma kuti aononge Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma akulu a ansembe ndi akuluakulu ananyengerera gulu la anthu kuti apemphe Baraba ndi kuti Yesu aphedwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ansembe akuru anapangira anthu kuti apemphe Baraba, koma kuti aononge Yesu.