Matthew 27:47 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atamva mauwo, ena amene adaaimirira pamenepo adati, “Munthuyu akuitana Eliya.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ena a iwo akuimirira komweko, pamene anamva, ananena, Uyo aitana Eliya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ena a oyimirira pamalopo atamva izi anati, “Akuyitana Eliya.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ena a iwo akuimirira komweko, pamene anamva, ananena, Uyo aitana Eliya.