Matthew 27:50 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Yesu adafuulanso kwakukulu, napereka mzimu wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesu, pamene anafuula ndi mau akulu, anapereka mzimu wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo pamene Yesu analiranso mofuwula, anapereka mzimu wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesu, 9 pamene anapfuula ndi mau akuru, anapereka mzimu wace.