Matthew 27:65 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pilato adaŵauza kuti, “Paja alonda muli nawo. Pitani, kalondeni pamandapo monga mukudziŵira.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pilato anati kwa iwo, Tengani alonda; mukani, kasungeni monga mudziwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pilato anayankha kuti, “Tengani mlonda kalondereni monga mudziwira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pilato anati kwa iwo, Tengani alonda; mukani, kasungeni monga mudziwa.