Matthew 27:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho adapangana kuti ndalamazo agulire munda wa mmisiri wa mbiya, kuti ukhale manda a alendo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma anapangana, nazigula munda wa woumba mbiya, ukhale manda a alendo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho anagwirizana kuti ndalamazo azigwiritse ntchito pogulira munda wa wowumba mbiya kuti ukhale manda alendo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma anapangana, nazigula munda wa woumba mbiya, ukhale manda a alendo.