Matthew 4:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu okhala mu mdima aona kuŵala kwakukulu. Anthu okhala m'dziko la mdima wabii wa imfa, kuŵala kwaŵaonekera.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
anthu akukhala mumdima adaona kuwala kwakukulu, ndi kwa iwo okhala m'malo a mthunzi wa imfa, kuwala kunatulukira iwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
anthu okhala mu mdima awona kuwala kwakukulu; ndi kwa iwo okhala mʼdziko la mthunzi wa imfa kuwunika kwawafikira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anthu akukhala mumdima Adaona kuwala kwakukuru, Ndi kwa iwo okhala m'malo mthunzi wa imfa, Kuwala kunaturukira iwo.