Matthew 5:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngodala anthu amene ali osauka mumtima mwao, pakuti Ufumu wakumwamba ndi wao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Odala ali osauka mumzimu; chifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Odala ndi amene ali osauka mu mzimu, chifukwa ufumu wakumwamba ndi wawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Odala ali osauka mumzimu; cifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba.