Matthew 5:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngodala anthu amene akumva chisoni, pakuti Mulungu adzaŵasangalatsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Odala ali achisoni; chifukwa adzasangalatsidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Odala ndi amene ali achisoni, chifukwa adzatonthozedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Odala ali acisoni; cifukwa adzasangalatsidwa.