Matthew 5:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngodala anthu oyera mtima, pakuti adzaona Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Odala ali oyera mtima; chifukwa adzaona Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Odala ndi amene ali oyera mtima, chifukwa adzaona Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Odala ali oyera mtima; cifukwa adzaona Mulungu.