Matthew 5:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngodala anthu odzetsa mtendere, pakuti Mulungu adzaŵatcha ana ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Odala ali akuchita mtendere; chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndi odala amene amabweretsa mtendere, chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Odala ali akucita mtendere; cifukwa adzachedwa ana a Mulungu.