Matthew 6:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo musalole kuti tigwe m'zotiyesa, koma mutipulumutse kwa Woipa uja.” [Pakuti ufumu, mphamvu ndi ulemerero ndi zanu kwamuyaya. Amen.]
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo musatitengere kokatiyesa; koma mutipulumutse kwa woyipayo.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.