Matthew 6:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma iwe, pamene ukusala zakudya, samba m'maso nkudzola mafuta kumutu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma pamene ukusala kudya, samba mʼmaso nudzole mafuta kumutu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako: