Matthew 7:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Musamaweruza anthu ena kuti ndi olakwa, kuwopa kuti Mulungu angakuweruzeni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musaweruze, kuti mungaweruzidwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Musaweruze ena, kuti inunso mungadzaweruzidwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musaweruze, kuti mungaweruzidwe.