Matthew 7:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
chifukwa ankaŵaphunzitsa monga munthu waulamuliro osati monga m'mene ankachitira aphunzitsi a Malamulo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti anawaphunzitsa monga mwini mphamvu, wosanga alembi ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
chifukwa anaphunzitsa ngati amene anali ndi ulamuliro osati ngati aphunzitsi amalamulo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti anawaphunzitsa monga mwini mphamvu, wosanga alembiao.