Matthew 7:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndani mwa inu, mwana wake atampempha buledi, iye nkumupatsa mwala?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndani mwa inu, mwana wake akamupempha buledi amamupatsa mwala?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wace mkate, adzampatsa mwala?