Matthew 9:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaloŵa m'chombo naoloka nyanja, nkukafika ku mzinda wakwao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Iye analowa m'ngalawa, naoloka, nadza kumudzi kwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu analowa mʼbwato nawoloka, ndipo anabwera ku mudzi wa kwawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Iye analowa m'ngalawa, naoloka, nadza kumudzi kwao.