Matthew 9:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu atamva zimenezo, adaŵayankha kuti, “Anthu amene ali bwino sasoŵa sing'anga ai, koma amene akudwala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo m'mene Yesu anamva anati, Olimba safuna sing'anga ai, koma odwala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu atamva, anati, “Munthu wamoyo safuna singʼanga ayi, koma wodwala.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo m'mene Yesu anamva anati, Olimba safuna sing'anga ai, koma odwala.